Masalimo 50:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti zamoyo zonse zakuthengo ndi zanga, ndi ng'ombe za pa mapiri zikwi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti zamoyo zonse za kuthengo ndi zanga, ndi ng'ombe za pa mapiri zikwi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Popeza kuti nyama iliyonse yam'nkhalango ndi yanga, pamodzi ndi nyama zonse zokhala ku mapiri ochuluka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 pakuti nyama iliyonse yakunkhalango ndi yanga ndiponso ngʼombe za ku mapiri ochuluka. Onani mutuwo |