Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 50:8 - Buku Lopatulika

8 Sindikudzudzula iwe chifukwa cha nsembe zako; popeza nsembe zako zopsereza zili pamaso panga chikhalire.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Sindikudzudzula iwe chifukwa cha nsembe zako; popeza nsembe zako zopsereza zili pamaso panga chikhalire.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 “Sindikudzudzulani chifukwa cha nsembe zanu, popeza kuti mumapereka nsembe zanu zopsereza kwa Ine nthaŵi zonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Sindikudzudzula chifukwa cha nsembe zako, kapena nsembe zako zopsereza zimene zili pamaso panga nthawi zonse.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 50:8
6 Mawu Ofanana  

Pakuti simukondwera ndi nsembe, mwenzi nditapereka; nsembe yopsereza simuikonda.


Pakuti ndikondwera nacho chifundo, si nsembe ai; ndi kumdziwa Mulungu kuposa nsembe zopsereza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa