Masalimo 50:7 - Buku Lopatulika7 Imvani, anthu anga, ndipo ndidzanena; Israele, ndipo ndidzachita mboni pa iwe, Ine Mulungu, ndine Mulungu wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Imvani, anthu anga, ndipo ndidzanena; Israele, ndipo ndidzachita mboni pa iwe, Ine Mulungu, ndine Mulungu wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Imvani anthu anga, Ine ndidzalankhula. Ndidzapereka umboni wokutsutsani inu Aisraele. Ine ndine Mulungu, Mulungu wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Imvani inu anthu anga, ndipo Ine ndidzayankhula, iwe Israeli, ndipo Ine ndidzayankhula mokutsutsa; ndine Mulungu, Mulungu wako. Onani mutuwo |
Ndipo Yehova anachitira umboni Israele ndi Yuda mwa dzanja la mneneri aliyense, ndi mlauli aliyense, ndi kuti, Bwererani kuleka ntchito zanu zoipa, nimusunge malamulo anga ndi malemba anga, monga mwa chilamulo chonse ndinachilamulira makolo anu, ndi kuchitumizira inu mwa dzanja la atumiki anga aneneri.