Masalimo 50:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo zakumwamba zionetsera chilungamo chake; pakuti Mulungu mwini wake ndiye woweruza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo zakumwamba zionetsera chilungamo chake; pakuti Mulungu mwini wake ndiye woweruza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Zamumlengalenga zikulalika chilungamo cha Mulungu, pakuti Iye mwini ndiye muweruzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo mayiko akumwamba akulengeza chilungamo chake, pakuti Mulungu mwini ndi woweruza. Onani mutuwo |