Masalimo 50:5 - Buku Lopatulika5 Mundisonkhanitsire okondedwa anga, amene anapangana ndi Ine ndi nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mundisonkhanitsire okondedwa anga; amene anapangana ndi Ine ndi nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Iye akuti, “Sonkhanitsani pamaso panga, anthu anga okhulupirika, amene adachita chipangano ndi Ine popereka nsembe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mundisonkhanitsire okhulupirika anga, amene anachita pangano ndi ine pochita nsembe. Onani mutuwo |