Masalimo 50:4 - Buku Lopatulika4 Kumwamba adzaitana zakumwamba, ndi dziko lapansi, kuti aweruze anthu ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Kumwamba adzaitana zakumwamba, ndi dziko lapansi, kuti aweruze anthu ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Amaitana zamumlengalenga ndi za pansi pano, kuti zichite umboni pamene akuweruza anthu ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iye akuyitanitsa zamumlengalenga ndi za pa dziko lapansi kuti aweruze anthu ake. Onani mutuwo |