Masalimo 5:6 - Buku Lopatulika6 Mudzaononga iwo akunena bodza; munthu wokhetsa mwazi ndi wachinyengo, Yehova anyansidwa naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Mudzaononga iwo akunena bodza; munthu wokhetsa mwazi ndi wachinyengo, Yehova anyansidwa naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Inu mumaŵaononga anthu olankhula zonama. Inu Chauta mumanyansidwa nawo anthu onyenga ndi opha anzao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mumawononga iwo amene amanena mabodza; anthu akupha ndi achinyengo, Yehova amanyansidwa nawo. Onani mutuwo |