Masalimo 5:5 - Buku Lopatulika5 Opusa sadzakhazikika pamaso panu, mudana nao onse akuchita zopanda pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Opusa sadzakhazikika pamaso panu, mudana nao onse akuchita zopanda pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Anthu onyada sangathe kuwonekera pamaso panu. Inu mumadana ndi anthu onse ochita zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Onyada sangathe kuyima pamaso panu; Inu mumadana ndi onse ochita zoyipa. Onani mutuwo |