Masalimo 49:7 - Buku Lopatulika7 kuombola mbale sangadzamuombole, kapena kumperekera dipo kwa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 kuombola mbale sangadzamuombole, kapena kumperekera dipo kwa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Zoonadi, palibe munthu amene angadziwombole, kapena kupatsa Mulungu mtengo wa moyo wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Palibe munthu amene angawombole moyo wa mnzake kapena kuperekera mnzake dipo kwa Mulungu. Onani mutuwo |