Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 49:8 - Buku Lopatulika

8 Popeza chiombolo cha moyo wao ncha mtengo wake wapatali, ndipo chilekeke nthawi zonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Popeza chiombolo cha moyo wao ncha mtengo wake wapatali, ndipo chilekeke nthawi zonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Popeza kuti choombolera moyo wa munthu ndi chamtengowapatali, ndipo sangathe kuchikwanitsa,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Dipo la moyo ndi la mtengowapatali, palibe malipiro amene angakwanire,

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 49:8
4 Mawu Ofanana  

Kapena, Mundilanditse m'dzanja la mdani? Kapena, Mundiombole m'dzanja la oopsa?


Chilikuti chifundo chanu chakale, Ambuye, munachilumbirira Davide pa chikhulupiriko chanu?


Pakuti munthu adzapindulanji, akalandira dziko lonse, nataya moyo wake? Kapena munthu adzaperekanji chosintha ndi moyo wake?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa