Masalimo 49:16 - Buku Lopatulika16 Usaope polemezedwa munthu, pochuluka ulemu wa nyumba yake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Usaope polemezedwa munthu, pochuluka ulemu wa nyumba yake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Usavutike munthu wina akamalemera, pamene chuma cha m'nyumba mwake chikukulirakulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Usavutike mu mtima pamene munthu akulemera, pamene ulemerero wa nyumba yake ukuchulukirachulukira; Onani mutuwo |