Masalimo 49:17 - Buku Lopatulika17 pakuti pomwalira iye sadzamuka nako kanthu kalikonse; ulemu wake sutsika naye kumtsata m'mbuyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 pakuti pomwalira iye sadzamuka nako kanthu kalikonse; ulemu wake sutsika naye kumtsata m'mbuyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Chifukwa pamene munthuyu amwalira, sadzatengapo kanthu. Chuma chake sichidzapita naye limodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Pakuti sadzatenga kanthu pamodzi naye pamene wamwalira, ulemerero wake sudzapita pamodzi naye. Onani mutuwo |