Masalimo 49:15 - Buku Lopatulika15 Koma Mulungu adzaombola moyo wanga kumphamvu ya manda. Pakuti adzandilandira ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma Mulungu adzaombola moyo wanga kumphamvu ya manda. Pakuti adzandilandira ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Koma Mulungu adzaombola moyo wanga ku ulamuliro wa manda, sindidzaopa, pakuti Iye adzandilandira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. Onani mutuwo |