Masalimo 48:4 - Buku Lopatulika4 Pakuti, taonani, mafumuwo anasonkhana, anapitira pamodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pakuti, taonani, mafumuwo anasonkhana, anapitira pamodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mafumu adasonkhana, adafuna kuuthira nkhondo pamodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pamene mafumu anasonkhana pamodzi, pamene anayendera pamodzi kudzalimbana nafe, Onani mutuwo |