Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 48:4 - Buku Lopatulika

4 Pakuti, taonani, mafumuwo anasonkhana, anapitira pamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Pakuti, taonani, mafumuwo anasonkhana, anapitira pamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mafumu adasonkhana, adafuna kuuthira nkhondo pamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Pamene mafumu anasonkhana pamodzi, pamene anayendera pamodzi kudzalimbana nafe,

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 48:4
12 Mawu Ofanana  

Koma mtima wa mfumu ya Aramu unavutika kwambiri pa ichicho, naitana anyamata ake, nanena nao, Kodi simudzandiuza wina wa ife wovomerezana ndi mfumu ya Israele ndani?


Popeza ati, Akalonga anga kodi sali onse mafumu?


Ndipo adzayankhanji amithenga a amitundu? Kuti Yehova wakhazikitsa Ziyoni, ndipo m'menemo anthu ake ovutidwa adzaona pobisalira.


Tsiku limenelo adzaimba nyimbo imeneyi m'dziko la Yuda, Ife tili ndi mzinda wolimba; Iye adzaika chipulumutso chikhale machemba ndi malinga.


Ndipo panali masiku a Ahazi, mwana wa Yotamu, mwana wa Uziya, mfumu ya Yuda, kuti Rezini, mfumu ya Aramu, ndi Peka, mwana wa Remaliya, mfumu ya Israele, anakwera kunka ku Yerusalemu, kumenyana nao; koma sanathe kuupambana.


Ndipo chinagwidwa chilombocho, ndi pamodzi nacho mneneri wonyenga amene adachita zizindikiro pamaso pake, zimene anasokeretsa nazo iwo amene adalandira lemba la chilombo, ndi iwo akulambira fano lake; iwo awiri anaponyedwa ali moyo m'nyanja yamoto yakutentha ndi sulufure:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa