Masalimo 48:3 - Buku Lopatulika3 Mulungu adziwika m'zinyumba zake ngati msanje. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mulungu adziwika m'zinyumba zake ngati msanje. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mulungu waonetsa kuti ndiye woteteza mzindawo, pakuti Iye amakhala m'kati mwa malinga ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mulungu ali mu malinga ake; Iye wadzionetsa yekha kuti ndiye malinga akewo. Onani mutuwo |