Masalimo 48:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti Mulungu ameneyo ndiye Mulungu wathu kunthawi za nthawi, adzatitsogolera kufikira imfa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti Mulungu ameneyo ndiye Mulungu wathu kunthawi za nthawi, adzatitsogolera kufikira imfa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Mudzati, “Mulungu wathu ndi wotere, ndi Mulungu wathu kuyambira muyaya mpaka muyaya. Iye adzakhala wotitsogolera nthaŵi zonse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pakuti Mulungu uyu ndi Mulungu wathu ku nthawi zosatha; Iye adzakhala mtsogoleri wathu mpaka ku mapeto. Onani mutuwo |