Masalimo 46:4 - Buku Lopatulika4 Pali mtsinje, ngalande zake zidzakondweretsa mzinda wa Mulungu. Malo oyera okhalamo Wam'mwambamwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pali mtsinje, ngalande zake zidzakondweretsa mudzi wa Mulungu. Malo oyera okhalamo Wam'mwambamwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Koma kuli mtsinje umene mifuleni yake imasangalatsa anthu amumzinda wa Mulungu, malo oyera okhalako Wopambanazonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kuli mtsinje umene njira zake za madzi zimasangalatsa mzinda wa Mulungu, malo oyera kumene Wammwambamwamba amakhalako. Onani mutuwo |