Masalimo 46:3 - Buku Lopatulika3 Chinkana madzi ake akokoma, nachita thovu, nagwedezeka mapiri ndi kudzala kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Chinkana madzi ake akokoma, nachita thovu, nagwedezeka mapiri ndi kudzala kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 ngakhale nyanja zikokome ndi kututuma. Ngakhale mapiri anjenjemere ndi kulindima kwa nyanja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 ngakhale madzi ake atakokoma ndi kuchita thovu, ngakhale mapiri agwedezeke ndi kukokoma kwake. Onani mutuwo |