Masalimo 46:2 - Buku Lopatulika2 Chifukwa chake sitidzachita mantha, lingakhale lisandulika dziko lapansi, angakhale mapiri asunthika, nakhala m'kati mwa nyanja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Chifukwa chake sitidzachita mantha, lingakhale lisandulika dziko lapansi, angakhale mapiri asunthika, nakhala m'kati mwa nyanja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Nchifukwa chake sitidzaopa ngakhale dziko lapansi lisinthike, ngakhale mapiri agwe pakati pa nyanja zozama, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Nʼchifukwa chake sitidzaopa ngakhale dziko lapansi lisunthike, ngakhale mapiri agwe pakati pa nyanja, Onani mutuwo |