Masalimo 46:5 - Buku Lopatulika5 Mulungu ali m'kati mwake, sudzasunthika, Mulungu adzauthandiza mbandakucha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mulungu ali m'kati mwake, sudzasunthika, Mulungu adzauthandiza mbandakucha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mulungu ali m'kati mwa mzindawo, sudzaonongeka konse. Mulungu adzauthandiza dzuŵa lisanatuluke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mulungu ali mʼkati mwake, iwo sudzagwa; Mulungu adzawuthandiza mmawa. Onani mutuwo |
Ndipo anati kwa ine, Wobadwa ndi munthu iwe, pano mpokhala mpando wachifumu wanga, mpoponda kumapazi anga, pomwe ndidzakhala pakati pa ana a Israele kosatha; ndi nyumba ya Israele siidzadetsanso dzina langa loyera, ngakhale iwo kapena mafumu ao, mwa chigololo chao, ndi mitembo ya mafumu ao pa misanje yao,