Masalimo 45:13 - Buku Lopatulika13 Mwana wamkazi wa mfumu ngwa ulemerero wonse m'kati mwa nyumba, zovala zake nza malukidwe agolide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Mwana wamkazi wa mfumu ngwa ulemerero wonse m'kati mwa nyumba, zovala zake nza malukidwe agolide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 ndi chuma chao chamitundumitundu. Mwana wamkazi wa mfumu ali m'chipinda mwake, wadzikongoletsa kwambiri, wavala zovala zoluka ndi thonje lagolide. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Wokongola kwambiri ndi mwana wa mfumu ali mʼchipinda mwake, chovala chake ndi cholukidwa ndi thonje ndi golide. Onani mutuwo |