Masalimo 45:14 - Buku Lopatulika14 Adzamtsogolera kwa mfumu wovala zamawangamawanga, anamwali anzake omtsata adzafika nao kwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Adzamtsogolera kwa mfumu wovala zamawangamawanga, anamwali anzake omtsata adzafika nao kwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Akupita naye kwa mfumu atavala zovala zamaluŵa, pamodzi ndi anamwali anzake omperekeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Atavala zovala zamaluwamaluwa akupita naye kwa mfumu; anamwali okhala naye akumutsatira ndipo abweretsedwa kwa inu. Onani mutuwo |