Masalimo 44:9 - Buku Lopatulika9 Koma mwatitaya, ndi kutinyazitsa; ndipo simutuluka nao makamu a nkhondo athu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma mwatitaya, ndi kutinyazitsa; ndipo simutuluka nao makamu a nkhondo athu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Komabe Inu mwatitaya, ndipo mwatitsitsa, simunapite nawo limodzi ankhondo athu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma tsopano mwatikana ndi kutichepetsa; Inu simupitanso ndi ankhondo athu. Onani mutuwo |