Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 44:8 - Buku Lopatulika

8 Mwa Mulungu tidzitamanda tsiku lonse, ndipo dzina lanu tidzaliyamika kosatha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Mwa Mulungu tidzitamanda tsiku lonse, ndipo dzina lanu tidzaliyamika kosatha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Takhala tikunyadira mphamvu za Mulungu nthaŵi zonse, ndipo tidzakuthokozani mpaka muyaya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Timanyadira mwa Mulungu wathu tsiku lonse, ndipo tidzatamanda dzina lanu kwamuyaya.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 44:8
8 Mawu Ofanana  

Ndipo anawapulumutsa m'dzanja la iye amene anawada, nawaombola kudzanja la mdani.


kuti ulemu wanga uimbire Inu, wosakhala chete. Yehova Mulungu wanga, ndidzakuyamikani nthawi zonse.


Moyo wanga udzatamanda Yehova; ofatsa adzakumva nadzakondwera.


Mwa Yehova mbeu yonse ya Israele idzalungamitsidwa ndi kudzikuza.


koma wakudzitamandira adzitamandire adzikweze umo, kuti ali wakuzindikira, ndi kundidziwa Ine, kuti ndine Yehova wakuchita zokoma mtima, chiweruziro, ndi chilungamo m'dziko lapansi, pakuti m'menemo ndikondwerera, ati Yehova.


Koma ngati iwe unenedwa Myuda, nukhazikika palamulo, nudzitamandira pa Mulungu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa