Masalimo 44:10 - Buku Lopatulika10 Mutibwereretsa kuthawa otisautsa, ndipo akudana nafe adzifunkhira okha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Mutibwereretsa kuthawa otisautsa, ndipo akudana nafe adzifunkhira okha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mwalola kuti amaliwongo athu atipirikitse, ndipo adani athu apeza zofunkha kwathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Munachititsa ife kubwerera mʼmbuyo pamaso pa mdani ndipo amene amadana nafe atilanda katundu. Onani mutuwo |