Masalimo 44:11 - Buku Lopatulika11 Mwatipereka ngati nkhosa zoyenera kuzidya; ndipo mwatibalalitsa mwa amitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Mwatipereka ngati nkhosa zoyenera kuzidya; ndipo mwatibalalitsa mwa amitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Inu mwatisandutsa nkhosa zokaphedwa, mwatibalalitsa pakati pa mitundu ina ya anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Inu munatipereka kuti tiwonongedwe monga nkhosa ndipo mwatibalalitsa pakati pa anthu a mitundu ina. Onani mutuwo |