Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 44:7 - Buku Lopatulika

7 Koma Inu munatipulumutsa kwa iwo akutsutsana nafe, ndipo akudana nafe, mudawachititsa manyazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Koma Inu munatipulumutsa kwa iwo akutsutsana nafe, ndipo akudana nafe, mudawachititsa manyazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Koma Inu mwandilanditsa kwa adani athu, mwaŵachititsa manyazi amene amadana nafe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 koma Inu mumatigonjetsera adani athu, mumachititsa manyazi amene amadana nafe.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 44:7
19 Mawu Ofanana  

Ndipo ndidzaikira anthu anga Israele malo, ndi kuwaoka kuti akakhale m'malo ao a iwo okha, osasunthikanso. Ndipo anthu a mphulupulu sadzawavutanso, monga poyamba paja,


Ndidzawaveka adani ake ndi manyazi; koma pa iyeyu korona wake adzamveka.


Natikwatula kwa otisautsa; pakuti chifundo chake nchosatha.


Yehova Ambuye, ndinu mphamvu ya chipulumutso changa, munandiphimba mutu wanga tsiku lakulimbana nkhondo.


Ndiye amene apatsa mafumu chipulumutso: Amene alanditsa Davide mtumiki wake kulupanga loipa.


Achite manyazi nadodome iwo akulondola moyo wanga kuti auononge. Abwerere m'mbuyo, nachite manyazi iwo okondwera kundichitira choipa.


Pamenepo anaopa kwakukulu, popanda chifukwa cha kuopa, pakuti Mulungu anamwaza mafupa a iwo akuzinga iwe; unawachititsa manyazi, pakuti Mulungu anawakaniza.


Koma ndidzachitira chifundo nyumba ya Yuda, ndi kuwapulumutsa mwa Ine Yehova Mulungu wao, osawapulumutsa ndi uta, kapena lupanga, kapena nkhondo ndi akavalo, kapena apakavalo.


Palibe munthu adzatha kuima pamaso pako masiku onse a moyo wako; monga ndinakhala ndi Mose momwemo ndidzakhala ndi iwe; sindidzakusowa, sindidzakusiya.


Ndipo Yoswa anagwira mafumu awa onse ndi dziko lao nthawi yomweyi; chifukwa Yehova Mulungu wa Israele anathirira Israele nkhondo.


Koma Yehova anati kwa Yoswa, Usaope chifukwa cha iwowa; pakuti mawa, dzuwa lino ndidzawapereka onse ophedwa pamaso pa Israele; udzawadula mitsindo akavalo ao, ndi kutentha agaleta ao ndi moto.


Ndipo pamene Yehova anawaukitsira oweruza, Yehova anakhala naye woweruzayo, nawapulumutsa m'dzanja la adani ao masiku onse a woweruzayo; pakuti Yehova anagwidwa chisoni pa kubuula kwao chifukwa cha iwo akuwapsinja ndi kuwatsendereza.


Ndi msonkhano wonse uno udzazindikira kuti Yehova sapulumutsa ndi lupanga, kapena ndi mkondo; pakuti Yehova ndiye mwini nkhondo, ndipo Iye adzakuperekani inu m'manja athu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa