Masalimo 44:7 - Buku Lopatulika7 Koma Inu munatipulumutsa kwa iwo akutsutsana nafe, ndipo akudana nafe, mudawachititsa manyazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma Inu munatipulumutsa kwa iwo akutsutsana nafe, ndipo akudana nafe, mudawachititsa manyazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma Inu mwandilanditsa kwa adani athu, mwaŵachititsa manyazi amene amadana nafe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 koma Inu mumatigonjetsera adani athu, mumachititsa manyazi amene amadana nafe. Onani mutuwo |