Masalimo 44:4 - Buku Lopatulika4 Inu ndinu mfumu yanga, Mulungu; lamulirani chipulumutso cha Yakobo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Inu ndinu mfumu yanga, Mulungu; lamulirani chipulumutso cha Yakobo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Inu ndinu Mfumu yanga ndi Mulungu wanga, amene mudampambanitsa Yakobe pa nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Inu ndinu Mfumu yanga ndi Mulungu wanga amene mumalamulira chigonjetso cha Yakobo. Onani mutuwo |