Masalimo 44:5 - Buku Lopatulika5 Mwa Inu tidzakankhira pansi otsutsana nafe, m'dzina lanu tidzapondereza akutiukira ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mwa Inu tidzakankhira pansi otsutsana nafe, m'dzina lanu tidzapondereza akutiukira ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndi thandizo lanu tidakantha adani athu. Ndi mphamvu zanu tidapondereza ogalukira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kudzera kwa inu ife timabweza adani athu; kudzera mʼdzina lanu timapondereza otiwukirawo. Onani mutuwo |