Masalimo 44:2 - Buku Lopatulika2 Inu munapirikitsa amitundu ndi dzanja lanu, koma iwowa munawaoka; munasautsa mitundu ya anthu, ndipo munawaingitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Inu munapirikitsa amitundu ndi dzanja lanu, koma iwowa munawaoka; munasautsa mitundu ya anthu, ndipo munawaingitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Inu mudapirikitsa mitundu ina ya anthu, koma makolo athu mudaŵakhazika m'dziko lao. Inu mudasautsa mitundu ina ya anthu, koma makolo athuwo Inu mudaŵapatsa ufulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndi dzanja lanu munathamangitsa mitundu ya anthu ena ndi kudzala makolo athu; Inu munakantha mitundu ya anthu, koma makolo athuwo Inu munawapatsa ufulu. Onani mutuwo |