Masalimo 43:3 - Buku Lopatulika3 Tumizirani kuunika kwanu ndi choonadi chanu zinditsogolere; zindifikitse kuphiri lanu loyera, kumene mukhala Inuko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Tumizirani kuunika kwanu ndi choonadi chanu zinditsogolere; zindifikitse kuphiri lanu loyera, kumene mukhala Inuko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tumizani kuŵala kwanu ndi choona chanu kuti zinditsogolere. Zindifikitse ku phiri lanu loyera, kumalo kokhala Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tumizani kuwunika kwanu ndi choonadi chanu kuti zinditsogolere; mulole kuti zindifikitse ku phiri lanu loyera, kumalo kumene inu mumakhala. Onani mutuwo |