Masalimo 43:2 - Buku Lopatulika2 Pakuti Inu ndinu Mulungu wa mphamvu yanga; mwanditayiranji? Ndimayenderanji woliralira chifukwa cha kundipsinja mdani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pakuti Inu ndinu Mulungu wa mphamvu yanga; mwanditayiranji? Ndimayenderanji woliralira chifukwa cha kundipsinja mdani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndithu Inu ndinu Mulungu wamphamvu amene ndimathaŵirako. Mwanditayiranji? Ndiziyenderanji ndilikulira chifukwa chondipsinja mdani wanga? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pajatu Inu Mulungu ndinu mphamvu zanga. Nʼchifukwa chiyani mwandikana ine? Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira, woponderezedwa ndi mdani? Onani mutuwo |