Masalimo 42:7 - Buku Lopatulika7 Madzi akuya aitanizana ndi madzi akuya, pa mkokomo wa matiti anu; mafunde onse a nyondonyondo anandimiza ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Madzi akuya aitanizana ndi madzi akuya, pa mkokomo wa matiti anu; mafunde onse a nyondonyondo anandimiza ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Madzi akuya akuitanizana ndi madzi akuyanso, mathithi anu akulindima kochititsa mantha. Mafunde anu ang'onoang'ono ndi akuluakulu omwe andimiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Madzi akuya akuyitana madzi akuya mu mkokomo wa mathithi anu; mafunde anu onse obwera mwamphamvu andimiza. Onani mutuwo |