Masalimo 42:6 - Buku Lopatulika6 Mulungu wanga, moyo wanga udziweramira m'kati mwanga; chifukwa chake ndikumbukira Inu m'dziko la Yordani, ndi mu Aheremoni, m'kaphiri ka Mizara. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Mulungu wanga, moyo wanga udziweramira m'kati mwanga; chifukwa chake ndikumbukira Inu m'dziko la Yordani, ndi mu Aheremoni, m'kaphiri ka Mizara. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndatayiratu mtima, nchifukwa chake ndikukumbukira Inu Mulungu, pamene ndili ku dziko la Yordani, ku Heremoni ndi ku phiri la Mizara. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mulungu wanga. Moyo wanga uli ndi chisoni mʼkati mwanga kotero ndidzakumbukira Inu kuchokera ku dziko la Yorodani, ku mitunda ya Herimoni kuchokera ku phiri la Mizara. Onani mutuwo |