Masalimo 42:2 - Buku Lopatulika2 Moyo wanga uli ndi ludzu la kwa Mulungu, la kwa Mulungu wamoyo. Ndikadze liti kuoneka pamaso pa Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Moyo wanga uli ndi ludzu la kwa Mulungu, la kwa Mulungu wamoyo. Ndikadze liti kuoneka pamaso pa Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mtima wanga ukumva ludzu lofuna Mulungu, Mulungu wamoyo. Kodi ndidzafika liti pamaso pa Mulungu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Mulungu, lofuna Mulungu wamoyo. Kodi ndipite liti kukakumana ndi Mulungu? Onani mutuwo |