Masalimo 40:9 - Buku Lopatulika9 Ndalalikira chilungamo mu msonkhano waukulu; onani, sindidzaletsa milomo yanga, mudziwa ndinu Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndalalikira chilungamo mu msonkhano waukulu; onani, sindidzaletsa milomo yanga, mudziwa ndinu Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndalalika uthenga wabwino wa chipulumutso chanu pa msonkhano waukulu. Sindidatseke pakamwa, monga mukudziŵa, Inu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndikulalikira uthenga wa chilungamo chanu mu msonkhano waukulu; sinditseka milomo yanga monga mukudziwa Inu Yehova. Onani mutuwo |