Masalimo 40:8 - Buku Lopatulika8 kuchita chikondwero chanu kundikonda, Mulungu wanga; ndipo malamulo anu ali m'kati mwamtima mwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 kuchita chikondwero chanu kundikonda, Mulungu wanga; ndipo malamulo anu ali m'kati mwamtima mwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ndimakonda kuchita zimene mumafuna, Inu Mulungu wanga, malamulo anu ali mumtima mwanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndikufuna kuchita chifuniro chanu, Inu Mulungu wanga; lamulo lanu lili mu mtima mwanga.” Onani mutuwo |