Masalimo 40:6 - Buku Lopatulika6 Nsembe ndi chopereka simukondwera nazo; mwanditsegula makutu. Nsembe yopsereza ndi yamachimo simunapemphe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Nsembe ndi chopereka simukondwera nazo; mwanditsegula makutu. Nsembe yopsereza ndi yamachimo simunapempha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Simudafune nsembe ndi zopereka, koma mwandipatsa makutu oti ndizimvera. Simudapemphe nsembe yopsereza ndi yopepesera machimo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Nsembe ndi zopereka Inu simuzifuna, koma makutu anga mwawatsekula; zopereka zopsereza ndi zopereka chifukwa cha tchimo Inu simunazipemphe. Onani mutuwo |