Masalimo 39:9 - Buku Lopatulika9 Ndinakhala duu, sindinatsegule pakamwa panga; chifukwa inu mudachichita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndinakhala duu, sindinatsegula pakamwa panga; chifukwa inu mudachichita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndine mbeŵeŵe, sinditsekula pakamwa panga, pakuti ndinu amene mwachita zimenezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ine ndinali chete; sindinatsekule pakamwa panga pakuti Inu ndinu amene mwachita zimenezi. Onani mutuwo |