Masalimo 39:8 - Buku Lopatulika8 Ndipulumutseni kwa zolakwa zanga zonse, musandiike ndikhale chotonza cha wopusa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipulumutseni kwa zolakwa zanga zonse, musandiike ndikhale chotonza cha wopusa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pulumutseni ku zolakwa zanga zonse. Musandisandutse chinthu chochinyodola zitsiru. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Pulumutseni ku zolakwa zanga zonse; musandisandutse chonyozeka kwa opusa. Onani mutuwo |