Masalimo 39:10 - Buku Lopatulika10 Mundichotsere chovutitsa chanu; pandithera ine chifukwa cha kulanga kwa dzanja lanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Mundichotsere chovutitsa chanu; pandithera ine chifukwa cha kulanga kwa dzanja lanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Chotsani chikoti chanu pa ine, ndatheratu chifukwa cha mkwapulo wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Chotsani mkwapulo wanu pa ine; ndagonjetsedwa ndi nkhonya ya dzanja lanu. Onani mutuwo |