Masalimo 39:3 - Buku Lopatulika3 Mtima wanga unatentha m'kati mwa ine; unayaka moto pakulingirira ine. Pamenepo ndinalankhula ndi lilime langa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mtima wanga unatentha m'kati mwa ine; unayaka moto pakulingirira ine. Pamenepo ndinalankhula ndi lilime langa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mtima wanga udavutika, ndipo pamene ndidasinkhasinkha, mtima wanga udangoyaka moto. Pompo ndidalankhula ndi mau akuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mtima wanga unatentha mʼkati mwanga, ndipo pamene ndinkalingalira, moto unayaka; kenaka ndinayankhula ndi lilime langa: Onani mutuwo |