Masalimo 39:2 - Buku Lopatulika2 Ndinatonthola osanena mau, ndinakhala chete osalawa chokoma; ndipo chisoni changa chinabuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndinatonthola osanena mau, ndinakhala chete osalawa chokoma; ndipo chisoni changa chinabuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Motero ndidakhala chete osalankhula kanthu, ndidakhala duu, koma popanda phindu, chifukwa mavuto anga ankangokulirakulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Koma pamene ndinali chete osanena ngakhale kanthu kalikonse kabwino mavuto anga anachulukirabe. Onani mutuwo |