Masalimo 39:13 - Buku Lopatulika13 Ndiloleni, kuti nditsitsimuke, ndisanamuke ndi kukhala kuli zii. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndiloleni, kuti nditsitsimuke, ndisanamuke ndi kukhala kuli zii. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Musandiyang'ane mwaukali, choncho ndidzatha kusangalala, ndisanafe ndi kuzimirira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Musandiyangʼane mwaukali, choncho ndidzatha kusangalala ndisanafe ndi kuyiwalika.” Onani mutuwo |