Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 40:1 - Buku Lopatulika

1 Kuyembekeza ndayembekeza Yehova; ndipo anandilola, namva kufuula kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Kuyembekeza ndayembekeza Yehova; ndipo anandilola, namva kufuula kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Ine ndidayembekeza Chauta ndi mtima wokhulupirira kuti adzandithandize. Adaŵeramira pansi kuyang'ana kwa ine, namva kulira kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mofatsa ndinadikira Yehova Iye anatembenukira kwa ine ndipo anamva kulira kwanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 40:1
7 Mawu Ofanana  

Popeza amanditcherera khutu lake, chifukwa chake ndidzaitanira Iye masiku anga onse.


Ambuye, imvani liu langa; makutu anu akhale chimverere mau a kupemba kwanga.


Maso a Yehova ali pa olungama mtima, ndipo makutu ake atchereza kulira kwao.


Khala chete mwa Yehova, numlindirire Iye; usavutike mtima chifukwa cha iye wolemerera m'njira yake, chifukwa cha munthu wakuchita chiwembu.


Mulungu wanga, tcherani khutu, nimumvere, tsegulani maso anu, nimupenye zopasuka zathu, ndi mzinda udatchedwawo dzina lanu; pakuti dzina lanu; pakuti sititula mapembedzero athu pamaso panu, chifukwa cha ntchito zathu zolungama, koma chifukwa cha zifundo zanu zochuluka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa