Masalimo 38:8 - Buku Lopatulika8 Ndafooka ine, ndipo ndachinjizidwa, ndabangula chifukwa cha kumyuka mtima wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndafooka ine, ndipo ndachinjizidwa, ndabangula chifukwa cha kumyuka mtima wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ndatheratu, ndipo ndatswanyika. Ndikubuula chifukwa cha kuvutika mu mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu; ndikubuwula ndi ululu wa mumtima. Onani mutuwo |