Masalimo 38:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti m'chuuno mwanga mutentha kwambiri; palibe pamoyo m'mnofu mwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti m'chuuno mwanga mutentha kwambiri; palibe pamoyo m'mnofu mwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Thupi langa likutentha kwambiri ndi malungo, ndipo lilibe nyonga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Msana wanga wagwidwa ndi ululu wosasimbika, mulibe thanzi mʼthupi langa. Onani mutuwo |