Masalimo 38:5 - Buku Lopatulika5 Mabala anga anunkha, adaola, chifukwa cha kupusa kwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mabala anga anunkha, adaola, chifukwa cha kupusa kwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mabala anga aola ndipo akununkha chifukwa cha kupusa kwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mabala anga akuwola ndipo akununkha chifukwa cha uchitsiru wa moyo wanga wauchimo. Onani mutuwo |