Masalimo 38:4 - Buku Lopatulika4 Pakuti mphulupulu zanga zapitirira pamutu panga; ndathodwa nazo monga ndi katundu wolemera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pakuti mphulupulu zanga zapitirira pamutu panga; ndathodwa nazo monga ndi katundu wolemera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Machimo anga andimiza msinkhu, akundilemera ngati katundu woposa mphamvu zanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kulakwa kwanga kwandipsinja ngati katundu wolemera kwambiri kuposa mphamvu zanga. Onani mutuwo |