Masalimo 38:3 - Buku Lopatulika3 Mumnofu mwanga mulibe chamoyo chifukwa cha ukali wanu; ndipo m'mafupa anga simuzizira, chifukwa cha cholakwa changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mumnofu mwanga mulibe chamoyo chifukwa cha ukali wanu; ndipo m'mafupa anga simuzizira, chifukwa cha cholakwa changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Thupi langa lilibe mphamvu chifukwa cha ukali wanu. M'nkhongono mwanga mwalobodoka chifukwa cha uchimo wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Chifukwa cha ukali wanu mulibe thanzi mʼthupi langa; mafupa anga alibe mphamvu chifukwa cha tchimo langa. Onani mutuwo |